YouVersion Logo
Search Icon

Mt. 19:21

Mt. 19:21 BLY-DC

Yesu adamuuza kuti, “Ngati ufuna kukhala wabwino kotheratu, pita, kagulitse zonse zimene uli nazo. Ndalama zake ukapatse anthu osauka, ndipo chuma udzachipeza Kumwamba. Kenaka ubwere, uzidzanditsata.”

Free Reading Plans and Devotionals related to Mt. 19:21