Mt. 18:2-3
Mt. 18:2-3 BLY-DC
Apo Yesu adaitana mwana namuimiritsa pakati pao, ndipo adati, “Ndithu ndikunenetsa kuti mukapanda kusintha ndi kusanduka ngati ana, simudzaloŵa konse mu Ufumu wakumwamba.
Apo Yesu adaitana mwana namuimiritsa pakati pao, ndipo adati, “Ndithu ndikunenetsa kuti mukapanda kusintha ndi kusanduka ngati ana, simudzaloŵa konse mu Ufumu wakumwamba.