YouVersion Logo
Search Icon

Mt. 14:16-17

Mt. 14:16-17 BLY-DC

Koma Yesu adaŵauza kuti, “Palibe chifukwa choti achokere. Inuyo apatseni chakudya.” Iwo adati, “Pano tili ndi buledi msanu yekha ndi nsomba ziŵiri, basi.”

Free Reading Plans and Devotionals related to Mt. 14:16-17