YouVersion Logo
Search Icon

Mt. 12:31

Mt. 12:31 BLY-DC

Nchifukwa chake ndikunenetsa kuti Mulungu adzakhululukira anthu tchimo lililonse, ngakhale mau achipongwe omunyoza Iyeyo. Koma munthu wochita chipongwe Mzimu Woyera, Mulungu sadzamkhululukira.

Free Reading Plans and Devotionals related to Mt. 12:31