YouVersion Logo
Search Icon

Lk. 10:41-42

Lk. 10:41-42 BLY-DC

Ambuye adati, “Iwe Marita iwe, ukutekeseka nkuvutika ndi zinthu zambiri, koma chofunika nchimodzi chokha. Maria ndiye wasankhula chinthu chopambana, ndipo chimenechi palibe wina angamlande ai.”

Free Reading Plans and Devotionals related to Lk. 10:41-42