YouVersion Logo
Search Icon

Yoh. 19:26-27

Yoh. 19:26-27 BLY-DC

Pamene Yesu adaona amai ake ndi wophunzira uja amene Iye ankamukonda kwambiri, akuimirira pafupi, adauza amai ake kuti, “Mai, nayu mwana wanu.” Adauzanso wophunzirayo kuti, “Naŵa amai ako.” Ndipo kuyambira pamenepo wophunzirayo adaŵatenga amaiwo kumakaŵasamala kwao.

Free Reading Plans and Devotionals related to Yoh. 19:26-27