Gen. 35:18
Gen. 35:18 BLY-DC
Tsono Rakele akumwalira kumene, akupuma mwaŵefuŵefu, kutsirizika, adamutcha mwanayo Benoni, koma bambo wake adamutcha Benjamini.
Tsono Rakele akumwalira kumene, akupuma mwaŵefuŵefu, kutsirizika, adamutcha mwanayo Benoni, koma bambo wake adamutcha Benjamini.