YouVersion Logo
Search Icon

Gen. 34:25

Gen. 34:25 BLY-DC

Patangopita masiku atatu, zilonda za kuumbala kuja zisanapole pa anthu aja, ana aŵiri a Yakobe, Simeoni ndi Levi, alongo ake a Dina, adatenga mikondo yao, nakaloŵa mosadziŵika mumzinda muja, nkukapha amuna onse.

Free Reading Plans and Devotionals related to Gen. 34:25