YouVersion Logo
Search Icon

Gen. 32:9

Gen. 32:9 BLY-DC

Pamenepo Yakobe adayamba kupemphera. Adati, “Mulungu wa kholo langa Abrahamu, Mulungu wa bambo wanga Isaki, mundimve ine! Inu Chauta mudandiwuza kuti, ‘Bwerera ku dziko lako, dziko la abale ako, ndidzasamala kuti zinthu zikuyendere bwino.’

Free Reading Plans and Devotionals related to Gen. 32:9