YouVersion Logo
Search Icon

Gen. 28:13

Gen. 28:13 BLY-DC

Chauta adaimirira pambali pake namuuza kuti, “Ine ndine Chauta, Mulungu wa Abrahamu ndi wa Isaki. Dziko ukugonapoli ndidzakupatsa iwe pamodzi ndi zidzukulu zako.