YouVersion Logo
Search Icon

Ntc. 2:44-45

Ntc. 2:44-45 BLY-DC

Okhulupirira onse anali amodzi, ndipo ankagaŵana zinthu zao. Ankagulitsa minda yao ndi katundu wao, ndalama zake nkumagaŵira onse, malinga ndi kusoŵa kwa aliyense.