YouVersion Logo
Search Icon

ZEKARIYA 8:13

ZEKARIYA 8:13 BLPB2014

Ndipo kudzachitika kuti, monga munali chotembereretsa mwa amitundu, inu nyumba ya Yuda, ndi nyumba ya Israele, momwemo ndidzakusungani, ndipo mudzakhala chodalitsa nacho; musaope, alimbike manja anu.

Free Reading Plans and Devotionals related to ZEKARIYA 8:13