YouVersion Logo
Search Icon

ZEKARIYA 12:10

ZEKARIYA 12:10 BLPB2014

Ndipo ndidzatsanulira pa nyumba ya Davide, ndi pa okhala m'Yerusalemu, mzimu wa chisomo ndi wakupembedza; ndipo adzandipenyera Ine amene anandipyoza; nadzamlira ngati munthu alira mwana wake mmodzi yekha, nadzammvera zowawa mtima, monga munthu amvera zowawa mtima mwana wake woyamba.

Free Reading Plans and Devotionals related to ZEKARIYA 12:10