YouVersion Logo
Search Icon

AROMA 6:17-18

AROMA 6:17-18 BLPB2014

Koma ayamikidwe Mulungu, kuti ngakhale mudakhala akapolo a uchimo, tsopano mwamvera ndi mtima makhalidwe aja a chiphunzitso chimene munaperekedweracho; ndipo pamene munamasulidwa kuuchimo, munakhala akapolo a chilungamo.

Free Reading Plans and Devotionals related to AROMA 6:17-18