YouVersion Logo
Search Icon

AROMA 6:13

AROMA 6:13 BLPB2014

ndipo musapereke ziwalo zanu kuuchimo, zikhale zida za chosalungama; koma mudzipereke inu nokha kwa Mulungu, monga amoyo atatuluka mwa akufa, ndi ziwalo zanu kwa Mulungu zikhale zida za chilungamo.

Free Reading Plans and Devotionals related to AROMA 6:13