YouVersion Logo
Search Icon

MATEYU 6:25

MATEYU 6:25 BLPB2014

Chifukwa chake ndinena kwa inu, Musadere nkhawa moyo wanu, chimene mudzadya ndi chimene mudzamwa; kapena thupi lanu, chimene mudzavala. Kodi moyo suli woposa chakudya, ndi thupi loposa chovala?

Video for MATEYU 6:25

Free Reading Plans and Devotionals related to MATEYU 6:25