YouVersion Logo
Search Icon

MATEYU 27:22-23

MATEYU 27:22-23 BLPB2014

Pilato ananena kwa iwo, Nanga ndidzachita chiyani ndi Yesu, wotchedwa Khristu? Onse anati, Apachikidwe pamtanda. Ndipo iye anati, Chifukwa ninji? Anachita choipa chotani? Koma iwo anafuulitsa kopambana, Apachikidwe pamtanda.

Free Reading Plans and Devotionals related to MATEYU 27:22-23