YouVersion Logo
Search Icon

MATEYU 19:29

MATEYU 19:29 BLPB2014

Ndipo onse amene adasiya nyumba, kapena abale, kapena alongo, kapena atate, kapena amai, kapena ana, kapena minda, chifukwa cha dzina langa, adzalandira zobwezeredwa zambirimbiri, nadzalowa moyo wosatha.

Free Reading Plans and Devotionals related to MATEYU 19:29