YouVersion Logo
Search Icon

MATEYU 17:20

MATEYU 17:20 BLPB2014

Ndipo Iye ananena kwa iwo, Chifukwa chikhulupiriro chanu nchaching'ono: pakuti indetu ndinena kwa inu, Mukakhala nacho chikhulupiriro monga kambeu kampiru, mudzati ndi phiri ili, Senderapo umuke kuja; ndipo lidzasendera; ndipo palibe kanthu kadzakukanikani.

Free Reading Plans and Devotionals related to MATEYU 17:20