YouVersion Logo
Search Icon

MATEYU 15:8-9

MATEYU 15:8-9 BLPB2014

Anthu awa andilemekeza Ine ndi milomo yao; koma mtima wao uli kutali ndi Ine. Koma andilambira Ine kwachabe, ndi kuphunzitsa maphunzitso, malangizo a anthu.