YouVersion Logo
Search Icon

MATEYU 14:16-17

MATEYU 14:16-17 BLPB2014

Koma Yesu anati kwa iwo, Iwo alibe chifukwa cha kumukira, apatseni ndinu adye. Koma iwo ananena kwa Iye, Ife tilibe kanthu pano koma mikate isanu, ndi nsomba ziwiri.

Free Reading Plans and Devotionals related to MATEYU 14:16-17