YouVersion Logo
Search Icon

MATEYU 13:44

MATEYU 13:44 BLPB2014

Ufumu wa Kumwamba uli wofanana ndi chuma chobisika m'munda; chimene munthu anachipeza, nachibisa; ndipo m'kuchikonda kwake achoka, nagulitsa zonse ali nazo, nagula munda umenewu.