YouVersion Logo
Search Icon

MALAKI 3:17-18

MALAKI 3:17-18 BLPB2014

Ndipo adzakhala angaanga, ati Yehova wa makamu, tsiku ndidzaikalo, ndipo ndidzawaleka monga munthu aleka mwana wake womtumikira. Pamenepo mudzabwera ndi kuzindikira pakati pa wolungama ndi woipa, pakati pa iye wotumikira Mulungu ndi iye wosamtumikira.

Video for MALAKI 3:17-18

Free Reading Plans and Devotionals related to MALAKI 3:17-18