YouVersion Logo
Search Icon

YOSWA 23:14

YOSWA 23:14 BLPB2014

Ndipo taonani, lero lino ndilikumuka njira ya dziko lonse lapansi; ndipo mudziwa m'mitima yanu yonse, ndi m'moyo mwa inu nonse, kuti pa mau okoma onse Yehova Mulungu wanu anawanena za inu sanagwe padera mau amodzi; onse anachitikira inu, sanasowepo mau amodzi.

Video for YOSWA 23:14

Free Reading Plans and Devotionals related to YOSWA 23:14