YOSWA 2:8-9
YOSWA 2:8-9 BLPB2014
Koma asanagone iwo, anawakwerera patsindwi iye, nati kwa amunawo, Ndidziwa kuti Yehova wakupatsani dzikoli, ndi kuti kuopsa kwanu kwatigwera, ndi kuti okhala m'dziko onse asungunuka pamaso panu.
Koma asanagone iwo, anawakwerera patsindwi iye, nati kwa amunawo, Ndidziwa kuti Yehova wakupatsani dzikoli, ndi kuti kuopsa kwanu kwatigwera, ndi kuti okhala m'dziko onse asungunuka pamaso panu.