YouVersion Logo
Search Icon

YOSWA 2:8-9

YOSWA 2:8-9 BLPB2014

Koma asanagone iwo, anawakwerera patsindwi iye, nati kwa amunawo, Ndidziwa kuti Yehova wakupatsani dzikoli, ndi kuti kuopsa kwanu kwatigwera, ndi kuti okhala m'dziko onse asungunuka pamaso panu.

Free Reading Plans and Devotionals related to YOSWA 2:8-9