YouVersion Logo
Search Icon

YOSWA 2:11

YOSWA 2:11 BLPB2014

Ndipo titamva ichi mitima yathu inasungunuka; analibenso mtima ndi mmodzi yense, chifukwa cha inu; pakuti Yehova Mulungu wanu, ndiye Mulungu wa m'mwamba umo, ndi pa dziko lapansi.

Free Reading Plans and Devotionals related to YOSWA 2:11