YouVersion Logo
Search Icon

YAKOBO 3:9-10

YAKOBO 3:9-10 BLPB2014

Timayamika Ambuye ndi Atate nalo; nalonso timatemberera anthu, okhala monga mwa mafanizidwe a Mulungu; Mochokera m'kamwa momwemo mutuluka chiyamiko ndi temberero. Abale anga, izi siziyenera kutero.