YouVersion Logo
Search Icon

YESAYA 63:7

YESAYA 63:7 BLPB2014

Ndidzatchula zachifundo chake cha Yehova, ndi matamando a Yehova, monga mwa zonse zimene Yehova wapereka kwa ife; ndi ubwino wake waukulu kwa banja la Israele, umene Iye wapereka kwa iwo, monga mwa chifundo chake, ndi monga mwa ntchito zochuluka za chikondi chake.

Free Reading Plans and Devotionals related to YESAYA 63:7