YouVersion Logo
Search Icon

YESAYA 53:8

YESAYA 53:8 BLPB2014

Anachotsedwa ku chipsinjo ndi chiweruziro; ndipo ndani adzafotokoza nthawi ya moyo wake? Pakuti walikhidwa kunja kuno; chifukwa cha kulakwa kwa anthu anga Iye anakhomedwa.

Free Reading Plans and Devotionals related to YESAYA 53:8