YouVersion Logo
Search Icon

YESAYA 53:2

YESAYA 53:2 BLPB2014

Pakuti ameneyo adzaphuka pamaso pake ngati mtengo wanthete, ndi ngati muzu womera m'nthaka youma; Iye alibe maonekedwe, pena kukongola; ndipo pamene timuona palibe kukongola kuti timkhumbe.

Free Reading Plans and Devotionals related to YESAYA 53:2