YouVersion Logo
Search Icon

HOSEYA 1:7

HOSEYA 1:7 BLPB2014

Koma ndidzachitira chifundo nyumba ya Yuda, ndi kuwapulumutsa mwa Ine Yehova Mulungu wao, osawapulumutsa ndi uta, kapena lupanga, kapena nkhondo ndi akavalo, kapena apakavalo.

Related Videos