YouVersion Logo
Search Icon

EZEKIELE 2:7-8

EZEKIELE 2:7-8 BLPB2014

Ndipo ukanene nao mau anga, ngakhale akamva kapena akaleka kumva; pakuti iwo ndiwo opanduka. Koma iwe, wobadwa ndi munthu, tamvera ichi ndilikunena nawe; usakhale iwe wopanduka, ngati nyumba ija yopanduka; tsegula pakamwa pako, nudye chomwe ndikupatsa.

Free Reading Plans and Devotionals related to EZEKIELE 2:7-8