YouVersion Logo
Search Icon

EKSODO 35:30-31

EKSODO 35:30-31 BLPB2014

Ndipo Mose anati kwa ana a Israele, Taonani, Yehova anaitana, ndi kumtchula dzina lake, Bezalele, mwana wa Uri, mwana wa Huri, wa fuko la Yuda; ndipo anamdzaza ndi mzimu wa Mulungu, ndi luso, ndi nzeru, ndi chidziwitso, za m'ntchito zilizonse

Free Reading Plans and Devotionals related to EKSODO 35:30-31