YouVersion Logo
Search Icon

EKSODO 29:45-46

EKSODO 29:45-46 BLPB2014

Ndipo ndidzakhala pakati pa ana a Israele, ndi kukhala Mulungu wao. Ndipo adzadziwa kuti Ine ndine Yehova Mulungu wao, amene ndinawatulutsa m'dziko la Ejipito, kuti ndikhale pakati pao. Ine ndine Yehova Mulungu wao.

Free Reading Plans and Devotionals related to EKSODO 29:45-46