YouVersion Logo
Search Icon

DANIELE 3:29

DANIELE 3:29 BLPB2014

Chifukwa chake ndilamulira kuti anthu ali onse, mtundu uliwonse, ndi a manenedwe ali onse, akunenera molakwira Mulungu wa Sadrake, Mesaki, ndi Abedenego, adzadulidwa nthulinthuli, ndi nyumba zao zidzasanduka dzala; popeza palibe mulungu wina akhoza kulanditsa motero.

Free Reading Plans and Devotionals related to DANIELE 3:29