YouVersion Logo
Search Icon

2 AKORINTO 3:5-6

2 AKORINTO 3:5-6 BLPB2014

si kuti tili okwanira pa ife tokha, kuyesera kanthu monga mochokera mwa ife tokha; kukwanira kwathu kuchokera kwa Mulungu; amenenso anatikwaniritsa ife tikhale atumiki a pangano latsopano; si la chilembo, koma la mzimu; pakuti chilembo chipha, koma mzimu uchititsa moyo.

Free Reading Plans and Devotionals related to 2 AKORINTO 3:5-6