YouVersion Logo
Search Icon

1 AKORINTO 9:25-26

1 AKORINTO 9:25-26 BLPB2014

Koma yense wakuyesetsana adzikanizira zonse. Ndipo iwowa atero kuti alandire korona wakuvunda; koma ife wosavunda. Chifukwa chake ine ndithamanga chotero, si monga chosinkhasinkha. Ndilimbana chotero, si monga ngati kupanda mlengalenga