1 AKORINTO 5:12-13
1 AKORINTO 5:12-13 BLPB2014
Pakuti nditani nao akunja kukaweruza iwo? Kodi amene ali m'katimo simuwaweruza ndi inu, koma akunja awaweruza Mulungu? Chotsani woipayo pakati pa inu nokha.
Pakuti nditani nao akunja kukaweruza iwo? Kodi amene ali m'katimo simuwaweruza ndi inu, koma akunja awaweruza Mulungu? Chotsani woipayo pakati pa inu nokha.