YouVersion Logo
Search Icon

1 AKORINTO 2:14

1 AKORINTO 2:14 BLPB2014

Koma munthu wa chibadwidwe cha umunthu salandira za Mzimu wa Mulungu: pakuti aziyesa zopusa; ndipo sakhoza kuzizindikira, chifukwa ziyesedwa mwauzimu.