YouVersion Logo
Search Icon

Zefaniya 3:20

Zefaniya 3:20 CCL

Pa nthawi imeneyo ndidzakusonkhanitsani; pa nthawi imeneyo ndidzakubweretsani ku mudzi kwanu. Ndidzakuyamikirani ndi kukuchitirani ulemu pakati pa mitundu ya anthu a dziko lapansi pamene ndidzabwezeretsa mtendere wanu inu mukuona,” akutero Yehova.

Free Reading Plans and Devotionals related to Zefaniya 3:20