YouVersion Logo
Search Icon

Miyambo 26:4-5

Miyambo 26:4-5 CCL

Usayankhe chitsiru monga mwa uchitsiru wake, kuopa kuti ungadzakhale ngati chitsirucho. Koma nthawi zina umuyankhe monga mwa uchitsiru wake, kuopa kuti angamadziyese yekha wanzeru.

Free Reading Plans and Devotionals related to Miyambo 26:4-5