YouVersion Logo
Search Icon

Miyambo 22:22-23

Miyambo 22:22-23 CCL

Mʼmphawi usamubere chifukwa ndi osauka, ndipo usawapondereze anthu osowa mʼbwalo la milandu, pakuti Yehova adzawateteza pa mlandu wawo ndipo adzalanda moyo onse amene amawalanda iwo.

Free Reading Plans and Devotionals related to Miyambo 22:22-23