YouVersion Logo
Search Icon

Afilipi 3:8

Afilipi 3:8 CCL

Kuwonjeza pamenepo, ndikuziona zonse kuti nʼzopanda phindu poyerekeza ndi phindu lopambana la kudziwa Khristu Yesu Ambuye anga. Nʼchifukwa cha Yesuyo ndataya zinthu zonse ndipo ndikuziyesa zinyalala kuti ndipindule Khristu

Free Reading Plans and Devotionals related to Afilipi 3:8