YouVersion Logo
Search Icon

Numeri 21:7

Numeri 21:7 CCL

Anthuwo anabwera kwa Mose ndi kunena kuti, “Tachimwa chifukwa tayankhula motsutsana ndi Yehova komanso inu. Pempherani kwa Yehova kuti atichotsere njokazi.” Tsono Mose anapempherera anthuwo.

Video for Numeri 21:7