YouVersion Logo
Search Icon

Numeri 14:6-7

Numeri 14:6-7 CCL

Yoswa mwana wa Nuni ndi Kalebe mwana wa Yefune, omwe anali amodzi mwa amene anakazonda nawo dziko, anangʼamba zovala zawo ndipo anati kwa gulu lonse la Aisraeli, “Dziko limene tinakayendamo ndi kuliona ndi labwino kwambiri zedi.

Free Reading Plans and Devotionals related to Numeri 14:6-7