YouVersion Logo
Search Icon

Numeri 13:32

Numeri 13:32 CCL

Choncho anthuwo anafalitsa pakati pa Aisraeli mbiri yoyipa ya dziko lomwe anakalionalo. Iwo anati, “Dziko limene tinapita kukalizonda limawononga anthu okhala mʼmenemo. Ndipo anthu onse amene tinakawaona kumeneko ndi ataliatali.

Video for Numeri 13:32

Free Reading Plans and Devotionals related to Numeri 13:32