YouVersion Logo
Search Icon

Marko 9:42

Marko 9:42 CCL

“Ndipo ngati wina aliyense achimwitsa mmodzi wa ana angʼono awa amene akhulupirira Ine, kukanakhala bwino kwa iye kuti aponyedwe mʼnyanja atamangiriridwa mwala waukulu mʼkhosi mwake.

Free Reading Plans and Devotionals related to Marko 9:42