YouVersion Logo
Search Icon

Marko 5:25-26

Marko 5:25-26 CCL

Pomwepo panali mayi amene amadwala nthenda yotaya magazi kwa zaka khumi ndi ziwiri. Iye anavutika kwambiri pamene asingʼanga ambiri ankamusamalira ndipo anagwiritsa ntchito zonse anali nazo, koma mʼmalo mochira, nthenda yake inkakulakulabe.

Free Reading Plans and Devotionals related to Marko 5:25-26