Marko 3:24-25
Marko 3:24-25 CCL
Ngati ufumu ugawanikana mwa iwo okha, ufumu umenewo sungakhalitse. Ngati nyumba igawanikana mwa iyo yokha, nyumba imeneyo singathe kuyima.
Ngati ufumu ugawanikana mwa iwo okha, ufumu umenewo sungakhalitse. Ngati nyumba igawanikana mwa iyo yokha, nyumba imeneyo singathe kuyima.