YouVersion Logo
Search Icon

Marko 16:4-5

Marko 16:4-5 CCL

Koma atakweza maso awo, anaona kuti mwala umene unali waukulu kwambiri wagubuduzidwa kale. Atalowa mʼmanda, anaona mnyamata atavala mwinjiro woyera atakhala ku mbali ya kumanja, ndipo iwo anachita mantha.

Free Reading Plans and Devotionals related to Marko 16:4-5